Udani
Kudabwa
Nthawi zina ndima dabwa
Wanga anthu momwe ama khala
Kubaba mtima wanga uma baba
Ubaba anthu zomwe ama panga
Kudana anthu awa ama dana
Sibanja ine mango khala
Mwina ndi nyanga zomwe wina ana panga
Kapena sinyanga nakuba kapena chabe nikaduka
Kamene kalengesa banthu bamozi kupeza vifukwa
Cifukwa mayeso fufuza koma sina peze cifukwa eh
Kunjako nko kudha macita mantha ndi khalidwe yawa
Udani waconco wacoka kuti ma lankhulana
Pempelo yanga niyoti izozo ma lalilane
Nanga cikondi munali naco cinapita kuti
Funso
Kudabwa
Nthawi zina ndima dabwa
Wanga anthu momwe ama khala
Kubaba mtima wanga uma baba
Ubaba anthu zomwe ama panga
Kudana anthu awa ama dana
Sibanja ine mango khala
Kumakhalila midesu
Ena akulila Yesu
Mundisamalile ana banja isa pwasuke tikhale ifeso
Ogwilizana despite what we facing I hope we don't break us ineo
Pemphelo yanga ndiyoti udani ulipo kuntima uthepo
Koma zukhala nga e sizotheka anthuwa afuna afepo
Udani waconco ku opya Ambuye kumwamba muyanganilepo
Kuma kangana pa zopanda phindu poka poka ena afepo
Anthu wa ndani aloza umbuli wa conci ine sina onepo
Kudabwa
Nthawi zina ndima dabwa
Wanga anthu momwe ama khala
Kubaba mtima wanga uma baba
Ubaba anthu zomwe ama panga
Kudana anthu awa ama dana
Sibanja ine mango khala
Nthawi zina ndima dabwa
Wanga anthu momwe ama khala
Kubaba mtima wanga uma baba
Ubaba anthu zomwe ama panga
Kudana anthu awa ama dana
Sibanja ine mango khala
Mwina ndi nyanga zomwe wina ana panga
Kapena sinyanga nakuba kapena chabe nikaduka
Kamene kalengesa banthu bamozi kupeza vifukwa
Cifukwa mayeso fufuza koma sina peze cifukwa eh
Kunjako nko kudha macita mantha ndi khalidwe yawa
Udani waconco wacoka kuti ma lankhulana
Pempelo yanga niyoti izozo ma lalilane
Nanga cikondi munali naco cinapita kuti
Funso
Kudabwa
Nthawi zina ndima dabwa
Wanga anthu momwe ama khala
Kubaba mtima wanga uma baba
Ubaba anthu zomwe ama panga
Kudana anthu awa ama dana
Sibanja ine mango khala
Kumakhalila midesu
Ena akulila Yesu
Mundisamalile ana banja isa pwasuke tikhale ifeso
Ogwilizana despite what we facing I hope we don't break us ineo
Pemphelo yanga ndiyoti udani ulipo kuntima uthepo
Koma zukhala nga e sizotheka anthuwa afuna afepo
Udani waconco ku opya Ambuye kumwamba muyanganilepo
Kuma kangana pa zopanda phindu poka poka ena afepo
Anthu wa ndani aloza umbuli wa conci ine sina onepo
Kudabwa
Nthawi zina ndima dabwa
Wanga anthu momwe ama khala
Kubaba mtima wanga uma baba
Ubaba anthu zomwe ama panga
Kudana anthu awa ama dana
Sibanja ine mango khala
Credits
Writer(s): Chimwemwe Zulu
Lyrics powered by www.musixmatch.com
Link
© 2024 All rights reserved. Rockol.com S.r.l. Website image policy
Rockol
- Rockol only uses images and photos made available for promotional purposes (“for press use”) by record companies, artist managements and p.r. agencies.
- Said images are used to exert a right to report and a finality of the criticism, in a degraded mode compliant to copyright laws, and exclusively inclosed in our own informative content.
- Only non-exclusive images addressed to newspaper use and, in general, copyright-free are accepted.
- Live photos are published when licensed by photographers whose copyright is quoted.
- Rockol is available to pay the right holder a fair fee should a published image’s author be unknown at the time of publishing.
Feedback
Please immediately report the presence of images possibly not compliant with the above cases so as to quickly verify an improper use: where confirmed, we would immediately proceed to their removal.